Eksodo 1:17 - Buku Lopatulika17 Koma anamwino anaopa Mulungu, ndipo sanachite monga mfumu ya Aejipito inawauza, koma analeka ana aamuna akhale ndi moyo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Koma anamwino anaopa Mulungu, ndipo sanachite monga mfumu ya Aejipito inawauza, koma analeka ana amuna akhale ndi moyo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Koma azambawo ankaopa Mulungu, kotero kuti mau a mfumu aja sadaŵasamale konse, ana aamunawo ankangoŵaleka amoyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Koma azambawo ankaopa Mulungu ndipo sanachite zimene mfumu ya Igupto inawawuza kuti achite. Iwo analeka ana aamuna kuti akhale ndi moyo. Onani mutuwo |