Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 1:13 - Buku Lopatulika

13 Ndipo Aejipito anawagwiritsa ana a Israele ntchito yosautsa;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Ndipo Aejipito anawagwiritsa ana a Israele ntchito yosautsa;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 ndipo ankaŵakakamiza mwankhalwe kugwira ntchito yaukapolo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 ndipo anawagwiritsa ntchito mwankhanza kwambiri.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 1:13
8 Mawu Ofanana  

Ndipo anati kwa Abramu, Dziwitsa ndithu kuti mbeu zako zidzakhala alendo m'dziko la eni, ndipo zidzatumikira iwo, ndipo iwo adzasautsa izo zaka mazana anai;


nalankhula nao monga mwa uphungu wa achinyamata, nati, Atate wanga analemeretsa goli lanu, koma ine ndidzaonjezerapo pa goli lanu; atate wanga anakukwapulani ndi zikoti, koma ine ndidzakukwapulani ndi zinkhanira.


Ndipo tsopano, popeza atate wanga anakusenzetsani goli lolemera, ine ndidzaonjezerapo pa goli lanu; atate wanga anakukwapulani ndi zikoti, koma ine ndidzakukwapulani ndi zinkhanira.


Anasanduliza mitima yao, kuti adane nao anthu ake, kuti achite monyenga ndi atumiki ake.


nawawitsa moyo wao ndi ntchito yolimba, ya dothi ndi ya njerwa, ndi ntchito zonse za pabwalo, ntchito zao zonse zimene anawagwiritsa nzosautsa.


Monga mkango wobangula ndi chilombo choyendayenda, momwemo mfumu yoipa ya anthu osauka.


Usamamweruza momzunza; koma uope Mulungu wako.


Koma Yehova anakutengani, nakutulutsani m'ng'anjo yamoto, mu Ejipito, mukhale kwa Iye anthu a cholowa chake, monga mukhala lero lino.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa