Danieli 9:5 - Buku Lopatulika5 tachimwa, tachita mphulupulu, tachita zoipa, tapanduka, kupatuka ndi kusiya maneno anu ndi maweruzo anu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 tachimwa, tachita mphulupulu, tachita zoipa, tapanduka, kupatuka ndi kusiya maneno anu ndi maweruzo anu; Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 tachimwa ndipo tachita zolakwa ndi zoyipa. Takuwukirani posiya malangizo ndi malamulo anu. Onani mutuwo |