Danieli 7:21 - Buku Lopatulika21 Ndinapenya, ndipo nyanga yomweyi inachita nkhondo ndi opatulikawo, niwagonjetsa, mpaka inadza Nkhalamba ya kale lomwe; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Ndinapenya, ndipo nyanga yomweyi inachita nkhondo ndi opatulikawo, niwalaka, mpaka inadza Nkhalamba ya kale lomwe; Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Ndikuyangʼanitsitsa, nyanga imeneyi inathira nkhondo anthu oyera mtima ndi kuwagonjetsa, Onani mutuwo |