Danieli 7:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo zilombo zotsalazo anazichotsera ulamuliro wao, koma anatalikitsa moyo wao, ukhalenso nyengo ndi nthawi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo zilombo zotsalazo anazichotsera ulamuliro wao, koma anatalikitsa moyo wao, ukhalenso nyengo ndi nthawi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Zirombo zina zija zinalandidwa ulamuliro wawo, koma zinaloledwa kukhala ndi moyo kwa kanthawi. Onani mutuwo |