Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Danieli 6:19 - Buku Lopatulika

19 Nilawira mamawa mfumu, nimuka mofulumira kudzenje la mikango.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 Nilawira mamawa mfumu, nimuka mofulumira kudzenje la mikango.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 Mʼbandakucha, mfumu inanyamuka ndi kufulumira kupita ku dzenje la mikango lija.

Onani mutuwo Koperani




Danieli 6:19
6 Mawu Ofanana  

Pamenepo mfumu inamuka kuchinyumba chake, nichezera kusala usikuwo, ngakhale zoimbitsa sanabwere nazo pamaso pake, ndi m'maso mwake munamuumira.


Ndipo poyandikira padzenje inafuula ndi mau achisoni mfumu, ninena, niti kwa Daniele, Daniele, mnyamata wa Mulungu wamoyo, kodi Mulungu wako, amene umtumikira kosalekeza, wakhoza kukulanditsa kwa mikango?


Ndipo popita tsiku la Sabata, mbandakucha, tsiku lakuyamba la sabata, anadza Maria wa Magadala, ndi Maria winayo, kudzaona manda.


Ndipo anadza kumanda mamawa tsiku loyamba la Sabata, litatuluka dzuwa.


ndinalibe mpumulo mu mzimu wanga, posapeza ine Tito mbale wanga; koma polawirana nao ndinanka ku Masedoniya.


Mwa ichi inenso, posalekereranso, ndinatuma kukazindikira chikhulupiriro chanu, kuti kapena woyesa akadakuyesani, ndipo chivuto chathu chikadakhala chopanda pake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa