Danieli 6:19 - Buku Lopatulika19 Nilawira mamawa mfumu, nimuka mofulumira kudzenje la mikango. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Nilawira mamawa mfumu, nimuka mofulumira kudzenje la mikango. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Mʼbandakucha, mfumu inanyamuka ndi kufulumira kupita ku dzenje la mikango lija. Onani mutuwo |