Danieli 6:11 - Buku Lopatulika11 Pamenepo anasonkhana anthu awa, napeza Daniele alikupemphera ndi kupembedza pamaso pa Mulungu wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Pamenepo anasonkhana anthu awa, napeza Daniele alikupemphera ndi kupembedza pamaso pa Mulungu wake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Ndipo anthu awa anapita pamodzi ndi kukapeza Danieli akupemphera ndi kupempha Mulungu wake kuti amuthandize. Onani mutuwo |