Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Danieli 5:31 - Buku Lopatulika

31 Ndipo Dariusi Mmedi analandira ufumuwo ali wa zaka makumi asanu ndi limodzi mphambu ziwiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

31 Ndipo Dariusi Mmedi analandira ufumuwo ali wa zaka makumi asanu ndi limodzi mphambu ziwiri.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

31 ndipo Dariyo Mmedi analanda ufumuwo ali ndi zaka 62.

Onani mutuwo Koperani




Danieli 5:31
6 Mawu Ofanana  

Ndipo ndidzatengera dzikolo mau anga onse amene ndinanenera ilo, mau onse olembedwa m'buku ili, amene Yeremiya wanenera mitundu yonse.


Ndakutchera iwe msampha, ndi iwenso wagwidwa, iwe Babiloni, ndipo sunadziwe, wapezeka, ndiponso wagwidwa, chifukwa walimbana ndi Yehova.


Ndipo ine, chaka choyamba cha Dariusi Mmedi, ndinauka kumlimbikitsa ndi kumkhazikitsa.


PERES, ufumu wanu wagawika, nuperekedwa kwa Amedi ndi Aperisi.


Kudamkomera Dariusi kuikira ufumuwo akalonga zana limodzi mphambu makumi awiri akhale m'madera onse a ufumu;


Chaka choyamba cha Dariusi mwana wa Ahasuwero, wa mbeu ya Amedi, amene anamlonga mfumu ya Ababiloni;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa