Danieli 4:7 - Buku Lopatulika7 Pamenepo anafika alembi, openda, Ababiloni, ndi alauli; ndipo ndinawafotokozera lotoli, koma sanandidziwitse kumasulira kwake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Pamenepo anafika alembi, openda, Ababiloni, ndi alauli; ndipo ndinawafotokozera lotoli, koma sanandidziwitse kumasulira kwake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Pamene amatsenga, owombeza, alawuli ndi amawula anabwera, ndinawafotokozera maloto, koma sanathe kunditanthauzira. Onani mutuwo |