Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Danieli 2:8 - Buku Lopatulika

8 Mfumu inayankha, niti, Ndidziwatu kuti mukunkhuniza dala, pakuona inu kuti chinthuchi chandichokera.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Mfumu inayankha, niti, Ndidziwatu kuti mukunkhuniza dala, pakuona inu kuti chinthuchi chandichokera.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Ndipo mfumu inayankha kuti, “Ine ndikudziwa kuti mukungozengereza kufuna kutaya nthawi chabe chifukwa mukuzindikira kuti izi ndi zimene ndatsimikiza kuchita.

Onani mutuwo Koperani




Danieli 2:8
4 Mawu Ofanana  

Nabwerezanso iwo kuyankha, nati, Mfumu ifotokozere anyamata ake lotoli, ndipo tidzaidziwitsa kumasulira kwake.


Koma mukapanda kundidziwitsa lotoli, mlandu wanu ndi umodzi; popeza mwapanganiranatu mau onama ndi oipa, kuwanena pamaso panga, mpaka idzasanduka nyengo; chifukwa chake mundifotokozere lotoli, momwemo ndidzadziwa kuti mudzandidziwitsa kumasulira kwake komwe.


akuchita machawi, popeza masiku ali oipa.


Muyendere munzeru ndi iwo akunja, kuchita machawi nthawi ingatayike.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa