Danieli 2:7 - Buku Lopatulika7 Nabwerezanso iwo kuyankha, nati, Mfumu ifotokozere anyamata ake lotoli, ndipo tidzaidziwitsa kumasulira kwake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Nabwerezanso iwo kuyankha, nati, Mfumu ifotokozere anyamata ake lotoli, ndipo tidzaidziwitsa kumasulira kwake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Iwo anayankhanso kachiwiri kuti, “Mfumu iwuze atumiki ake chimene yalota, ndipo ife tidzatanthauzira.” Onani mutuwo |