Danieli 2:32 - Buku Lopatulika32 Fano ili tsono, mutu wake unali wagolide wabwino, chifuwa chake ndi manja ake zasiliva, mimba yake ndi chuuno chake zamkuwa, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 Fano ili tsono, mutu wake unali wagolide wabwino, chifuwa chake ndi manja ake zasiliva, mimba yake ndi chuuno chake zamkuwa, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 Mutu wa chowumbacho unali wagolide wabwino kwambiri. Chifuwa ndi manja ake zinali zasiliva. Mimba ndi ntchafu zake zinali zamkuwa. Onani mutuwo |