Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Danieli 2:3 - Buku Lopatulika

3 Niti nao mfumu, Ndalota loto, nuvutika mzimu wanga kudziwa lotolo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Niti nao mfumu, Ndalota loto, nuvutika mzimu wanga kudziwa lotolo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 mfumuyo inawawuza kuti, “Ndalota loto lomwe likundisautsa ndipo ndikufuna kudziwa tanthauzo lake.”

Onani mutuwo Koperani




Danieli 2:3
5 Mawu Ofanana  

Ndipo iwo anati kwa iye, Ife talota maloto, ndipo tilibe wotimasulira. Ndipo Yosefe anati kwa iwo, Kodi Mwini kumasulira si ndiye Mulungu? Mundifotokozeretu.


Farao ndipo anati kwa Yosefe, Ine ndalota loto, koma palibe wondimasulira; ndipo ndamva alikunena za iwe kuti, ukamva loto udziwa kumasulira.


Ndipo panali m'mamawa mtima wake unavutidwa; ndipo anatumiza naitana amatsenga onse a mu Ejipito, ndi anzeru onse a momwemo: ndipo Farao anafotokozera iwo loto lake; koma panalibe mmodzi anakhoza kuwamasulira iwo kwa Farao.


Chaka chachiwiri cha Nebukadinezara mfumu, Nebukadinezarayo analota maloto, ndi mzimu wake unavutika, ndi tulo take tidamwazikira.


Ndinaona loto lakundiopsa, ndi zolingirira za pakama panga, ndi masomphenya a m'mtima mwanga, zinandivuta ine.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa