Danieli 2:3 - Buku Lopatulika3 Niti nao mfumu, Ndalota loto, nuvutika mzimu wanga kudziwa lotolo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Niti nao mfumu, Ndalota loto, nuvutika mzimu wanga kudziwa lotolo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 mfumuyo inawawuza kuti, “Ndalota loto lomwe likundisautsa ndipo ndikufuna kudziwa tanthauzo lake.” Onani mutuwo |