Danieli 2:22 - Buku Lopatulika22 Iye avumbulutsa zinthu zakuya ndi zinsinsi; adziwa zokhala mumdima, ndi kuunika kumakhala kwa Iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Iye avumbulutsa zinthu zakuya ndi zinsinsi; adziwa zokhala mumdima, ndi kuunika kumakhala kwa Iye. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Amavumbulutsa zinthu zozama ndi zobisika; amadziwa zimene zili mu mdima, ndipo kuwunika kumakhala ndi Iye. Onani mutuwo |