Danieli 2:12 - Buku Lopatulika12 Chifukwa chake mfumu inakwiya, nizaza kwambiri, nilamulira kuti awaphe anzeru onse mu Babiloni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Chifukwa chake mfumu inakwiya, nizaza kwambiri, nilamulira kuti awaphe anzeru onse m'Babiloni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Zimenezi zinapsetsa mtima mfumu ndipo inakwiya kwambiri kotero inalamula kuti anzeru onse a ku Babuloni aphedwe. Onani mutuwo |