Danieli 12:8 - Buku Lopatulika8 Ndinachimva ichi, koma osachizindikira; pamenepo ndinati Mbuye wanga, chitsiriziro cha izi nchiyani? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndinachimva ichi, koma osachizindikira; pamenepo ndinati Mbuye wanga, chitsiriziro cha izi nchiyani? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Ndinamva, koma sindinamvetsetse. Choncho ndinafunsa kuti, “Mbuye wanga, nanga matsiriziro a zonsezi adzakhala chiyani?” Onani mutuwo |