Danieli 11:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo adzalowa mu ufumu wa mfumu ya kumwera, koma adzabwera m'dziko lakelake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo adzalowa m'ufumu wa mfumu ya kumwera, koma adzabwera m'dziko lakelake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Kenaka mfumu ya kumpoto idzathira nkhondo dziko la mfumu ya kummwera koma idzalephera ndi kubwerera kwawo. Onani mutuwo |