Danieli 1:11 - Buku Lopatulika11 Nati Daniele kwa kapitao, amene mkulu wa adindo adamuikayo ayang'anire Daniele, Hananiya, Misaele, ndi Azariya, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Nati Daniele kwa kapitao, amene mkulu wa adindo adamuikayo ayang'anire Daniele, Hananiya, Misaele, ndi Azariya, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Ndipo Danieli anati kwa kapitawo amene anali mkulu wa nduna za mfumu amene anamuyika kuti ayangʼanire Danieli, Hananiya, Misaeli ndi Azariya, Onani mutuwo |