Chivumbulutso 4:2 - Buku Lopatulika2 Pomwepo ndinakhala mwa Mzimu; ndipo, taonani padaikika mpando wachifumu mu Mwamba ndi pa mpandowo padakhala wina; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Pomwepo ndinakhala mwa Mzimu; ndipo, taonani padaikika mpando wachifumu m'Mwamba ndi pa mpandowo padakhala wina; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Nthaŵi yomweyo ndidagwidwa ndi Mzimu Woyera. Kumwambako ndidaona mpando wachifumu, wina atakhalapo pampandopo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Nthawi yomweyo ndinatengedwa ndi Mzimu Woyera, ndipo patsogolo panga ndinaona mpando waufumu wina atakhalapo. Onani mutuwo |