Amosi 8:6 - Buku Lopatulika6 kuti tigule osauka ndi ndalama, ndi aumphawi ndi nsapato, ndi kugulitsa nsadwa za tirigu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 kuti tigule osauka ndi ndalama, ndi aumphawi ndi nsapato, ndi kugulitsa nsadwa za tirigu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 kuti osauka tiŵagule ndi siliva, amphaŵi tiŵagule ndi nkhwaŵiro, kutinso tigulitse ndi mungu womwe wa tirigu?’ ” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 tigule osauka ndi ndalama zasiliva ndi osowa powapatsa nsapato, tigulitse ngakhale mungu wa tirigu?” Onani mutuwo |