Amosi 7:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo kunachitika m'mene lidatha kudya msipu wa dziko, ndinati, Ambuye Yehova, khululukiranitu Yakobo; adzakhala chilili bwanji? Popeza ndiye wamng'ono. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo kunachitika m'mene lidatha kudya msipu wa dziko, ndinati, Ambuye Yehova, khululukiranitu Yakobo; adzakhala chilili bwanji? Popeza ndiye wamng'ono. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Pamene ndidaona kuti dzombelo ladya zomera zonse zam'dzikomo, ndidati, “Inu Ambuye Chauta, ndapota nanu, khululukani. Kodi anthu a Yakobeŵa angalimbike bwanji? Iwoŵa ndi ofooka kwambiri.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Dzombelo litadya zomera zonse za mʼdzikomo, Ine ndinafuwula kuti, “Ambuye Yehova, khululukani! Kodi Yakobo adzapulumuka bwanji? Iye ndi wofowoka kwambiri!” Onani mutuwo |