Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Amosi 2:12 - Buku Lopatulika

12 Koma munamwetsa Anaziri vinyo, ndi kulamulira aneneri ndi kuti, Musamanenera.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Koma munamwetsa Anaziri vinyo, ndi kulamulira aneneri ndi kuti, Musamanenera.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 “Koma Inu mudaŵamwetsa vinyo Anaziri aja, ndipo mudaŵalamula aneneriwo kuti, ‘Musalose.’

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 “Koma inu munawamwetsa vinyo anaziri aja, ndipo munalamula aneneri kuti asanenere.

Onani mutuwo Koperani




Amosi 2:12
8 Mawu Ofanana  

amene amati kwa alauli, Mtima wanu usapenye; ndi kwa aneneri, Musanenere kwa ife zinthu zoona, munene kwa ife zinthu zamyadi, munenere zonyenga;


Chifukwa chake atero Yehova za anthu a Anatoti, amene afuna moyo wanga, kuti, Usanenere m'dzina la Yehova, ungafe ndi mkono wathu;


ndipo ndinaika pamaso pa ana aamuna a nyumba ya Arekabu mbale zodzala ndi vinyo, ndi zikho, ndipo ndinati kwa iwo, Imwani vinyo.


koma usaneneranso ku Betele; pakuti pamenepo mpamalo opatulika a mfumu, ndiyo nyumba yachifumu.


Chifukwa chake tsono, tamvera mau a Yehova, Iwe ukuti, Usamanenera chotsutsana ndi Israele, usadonthetsa mau akutsutsana ndi nyumba ya Isaki;


Musamanenera, amanenera ati. Sadzanenera kwa awa; matonzo sadzachoka.


Nena ndi ana a Israele, nuti nao, Mwamuna kapena mkazi akadzipatulira kulonjeza chowinda cha Mnaziri, kudzipatulira kwa Yehova;


azisala vinyo ndi kachasu; asamwe vinyo wosasa, kapena kachasu wosasa, kapena chakumwa chonse cha mphesa, asamwe; asadye mphesa zaziwisi kapena zouma.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa