Amosi 2:12 - Buku Lopatulika12 Koma munamwetsa Anaziri vinyo, ndi kulamulira aneneri ndi kuti, Musamanenera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Koma munamwetsa Anaziri vinyo, ndi kulamulira aneneri ndi kuti, Musamanenera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 “Koma Inu mudaŵamwetsa vinyo Anaziri aja, ndipo mudaŵalamula aneneriwo kuti, ‘Musalose.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 “Koma inu munawamwetsa vinyo anaziri aja, ndipo munalamula aneneri kuti asanenere. Onani mutuwo |