Akolose 3:3 - Buku Lopatulika3 Pakuti munafa, ndipo moyo wanu wabisika pamodzi ndi Khristu mwa Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Pakuti munafa, ndipo moyo wanu wabisika pamodzi ndi Khristu mwa Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Pakuti kunena za moyo wakalewo mudafa, ndipo moyo wanu watsopano ndi wobisika pamodzi ndi Khristu mwa Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Pakuti munafa, ndipo moyo wanu tsopano wabisika pamodzi ndi Khristu mwa Mulungu. Onani mutuwo |