Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Akolose 3:21 - Buku Lopatulika

21 Atate inu, musaputa ana anu, kuti angataye mtima.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

21 Atate inu, musaputa ana anu, kuti angataye mtima.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

21 Inu atate, musamaŵapsetsa mtima ana anu, kuti angataye mtima.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

21 Inu abambo, musakwiyitse ana anu, kuti angataye mtima.

Onani mutuwo Koperani




Akolose 3:21
7 Mawu Ofanana  

Monga atate achitira ana ake chifundo, Yehova achitira chifundo iwo akumuopa Iye.


pakuti Yehova adzudzula omwe awakonda; monga atate mwana amene akondwera naye.


Ndipo atate inu, musakwiyitse ana anu; komatu muwalere iwo m'maleredwe ndi chilangizo cha Ambuye.


Akapolo inu, mverani m'zonse iwo amene ali ambuye monga mwa thupi, wosati ukapolo wa pamaso, monga okondweretsa anthu, komatu ndi mtima wakulinga kumodzi, akuopa Ambuye;


monga mudziwa kuti tinachitira yense wa inu pa yekha, monga atate achitira ana ake a iye yekha,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa