Akolose 3:10 - Buku Lopatulika10 ndipo munavala watsopano, amene alikukonzeka watsopano, kuti akhale nacho chizindikiritso, monga mwa chifaniziro cha Iye amene anamlenga iye; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 ndipo munavala watsopano, amene alikukonzeka watsopano, kuti akhale nacho chizindikiritso, monga mwa chifaniziro cha Iye amene anamlenga iye; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 ndipo mwavala moyo watsopano. Moyo umenewu, Mlengi wanu akuukonzabe kosalekeza, kuti mudzamdziŵe kwenikweni ndi kufanafana naye. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 ndipo mwavala munthu watsopano, amene nzeru zake zikukonzedwanso kuti afanane ndi Mlengi wake. Onani mutuwo |