Akolose 2:22 - Buku Lopatulika22 (ndizo zonse zakuonongedwa pochita nazo), monga mwa malangizo ndi maphunziro a anthu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 (ndizo zonse zakuonongedwa pochita nazo), monga mwa malangizo ndi maphunziro a anthu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Malamulo ameneŵa ndi zophunzitsa zimenezi ndi za anthu chabe, ndipo zimangokhudza zinthu zimene zimatha, anthu akamazigwiritsa ntchito. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Malamulo amenewa amakhudza zinthu zimene zimatha zikamagwiritsidwa ntchito, ndipo malamulo ndi zophunzitsa za anthu chabe. Onani mutuwo |