Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Akolose 2:21 - Buku Lopatulika

21 usaikapo dzanja, usalawa, usakhudza,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

21 usaikapo dzanja, usalawa, usakhudza,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

21 “Usagwire chakuti”, “Usakhudze chakuti”?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

21 “Usagwire chakuti,” “Usalawe chakuti,” “Usakhudze chakuti?”

Onani mutuwo Koperani




Akolose 2:21
6 Mawu Ofanana  

Koma zipatso za mtengo umene uli m'kati mwa munda, Mulungu anati, Musadye umenewo, musakhudze umenewo, mungadzafe.


Chokani inu, chokani inu, tulukani ku Babiloni; musakhudze kanthu kodetsa; tulukani pakati pake, khalani okonzeka, inu amene munyamula zotengera za Yehova.


Chifukwa chake, Tulukani pakati pao, ndipo patukani, ati Ambuye, Ndipo musakhudza kanthu kosakonzeka; ndipo Ine ndidzalandira inu,


Ngati munafa pamodzi ndi Khristu kusiyana nazo zoyamba za dziko lapansi, mugonjeranji kuzoikikazo, monga ngati moyo wanu mukhala nao m'dziko lapansi,


(ndizo zonse zakuonongedwa pochita nazo), monga mwa malangizo ndi maphunziro a anthu?


a kuletsa ukwati, osiyitsa zakudya zakuti, zimene Mulungu anazilenga kuti achikhulupiriro ndi ozindikira choonadi azilandire ndi chiyamiko.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa