Akolose 2:15 - Buku Lopatulika15 atavula maukulu ndi maulamuliro, anawaonetsera poyera, nawagonjetsera nako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 atavula maukulu ndi maulamuliro, anawaonetsera poyera, nawagonjetsera nako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Motero mwa Khristu Mulungu adaŵalanda zida maufumu ndi maulamuliro onse, ndipo pamaso pa onse, adaŵayendetsa ngati akaidi pa mdipiti wokondwerera kupambana kwake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Ndipo atalanda zida maufumu ndi maulamuliro, Iye anawachititsa manyazi powayendetsa pamaso pa anthu onse atawagonjetsa ndi mtanda. Onani mutuwo |