Akolose 2:1 - Buku Lopatulika1 Pakuti ndifuna kuti inu mudziwe nkhawa imene ndili nayo chifukwa cha inu, ndi iwowa a mu Laodikea, ndi onse amene sanaone nkhope yanga m'thupi; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Pakuti ndifuna kuti inu mudziwe nkhawa imene ndili nayo chifukwa cha inu, ndi iwowa a m'Laodikea, ndi onse amene sanaone nkhope yanga m'thupi; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Ndikufuna kuti mudziŵe kuti ndikukuvutikirani kwambiri, inuyo ndi anzanu a ku Laodikea, ndi ena onse amene sitidaonane nawo maso ndi maso chikhalire. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Ndikufuna mudziwe kuti ndikukuvutikirani kwambiri, inuyo pamodzi ndi anzanu a ku Laodikaya, ndi ena onse amene sitinaonane maso ndi maso. Onani mutuwo |