Akolose 1:29 - Buku Lopatulika29 kuchita ichi ndidzivutitsa ndi kuyesetsa monga mwa machitidwe ake akuchita mwa ine ndi mphamvu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 kuchita ichi ndidzivutitsa ndi kuyesetsa monga mwa machitidwe ake akuchita mwa ine ndi mphamvu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Ndi cholinga chimenechi ndikugwiradi ntchito kwambiri ndi mphamvu ya Khristu imene ikugwira ntchito kolimba mwa ine. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Ndi cholinga chimenechi, ine ndikugwira ntchito molimbika ndi mwamphamvu zonse zimene Iye anachita mwa ine. Onani mutuwo |