Akolose 1:5 - Buku Lopatulika5 chifukwa cha chiyembekezo chosungikira kwa inu mu Mwamba, chimene mudachimva kale m'mau a choonadi cha Uthenga Wabwino, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 chifukwa cha chiyembekezo chosungikira kwa inu m'Mwamba, chimene mudachimva kale m'mau a choonadi cha Uthenga Wabwino, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Gwero la zonsezi ndi chiyembekezo chimene muli nacho chodzalandira zimene Mulungu akukusungirani Kumwamba. Mudamva za zimenezi pamene mau oona, adakufikani poyamba paja. Mau oonawo ndi Uthenga Wabwino. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Chikhulupiriro ndi chikondi, gwero lake ndi chiyembekezo chomwe muli nacho chodzalandira zimene anakusungirani kumwamba. Munamva kale za zimenezi kudzera mʼmawu a choonadi, Uthenga Wabwino Onani mutuwo |