Akolose 1:25 - Buku Lopatulika25 amene ndinakhala mtumiki wake, monga mwa udindo wa Mulungu umene anandipatsa ine wakuchitira inu, wakukwaniritsa mau a Mulungu, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 amene ndinakhala mtumiki wake, monga mwa udindo wa Mulungu umene anandipatsa ine wakuchitira inu, wakukwaniritsa mau a Mulungu, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Ndipo ine ndine mtumiki wa Mpingowu, pakuti Mulungu ndiye adandipatsa ntchitoyi yoti ndikulalikireni kwathunthu mau ake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Ine ndakhala mtumiki wake mwa lamulo limene Mulungu anandipatsa kuti ndipereke Mawu a Mulungu athunthu, Onani mutuwo |