Akolose 1:21 - Buku Lopatulika21 Ndipo inu, okhala alendo kale ndi adani m'chifuwa chanu m'ntchito zoipazo, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Ndipo inu, okhala alendo kale ndi adani m'chifuwa chanu m'ntchito zoipazo, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Kale inu munali kutali ndi Mulungu, ndipo munkadana naye m'maganizo anu ndi m'ntchito zanu zoipa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Kale inu munali kutali ndi Mulungu ndipo munali adani a Mulungu mʼmaganizo mwanu chifukwa cha khalidwe lanu loyipa. Onani mutuwo |