Ahebri 9:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo izi zitakonzeka kotero, ansembe amalowa m'chihema choyamba kosalekeza, ndi kutsiriza kulambirako; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo izi zitakonzeka kotero, ansembe amalowa m'chihema choyamba kosalekeza, ndi kutsiriza kulambirako; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Malinga ndi malongosoledwe ameneŵa, ansembe amaloŵa m'chipinda choyamba chija masiku onse pokagwira ntchito zao za chipembedzo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Zinthu zonsezi zitakonzedwa, ansembe ankalowamo mʼchipinda choyamba chija nthawi ndi nthawi kumatumikiramo. Onani mutuwo |