Ahebri 7:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo kuli ngati kunena, mwa Abrahamu Levinso wakulandira limodzilimodzi la magawo khumi adapereka limodzi la magawo khumi; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo kuli ngati kunena, mwa Abrahamu Levinso wakulandira limodzilimodzi la magawo khumi adapereka limodzi la magawo khumi; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Kwenikweni tingathe kunena kuti pamene Abrahamu ankapereka chachikhumi, Levi yemwe, amene amalandira chachikhumi, adaapereka nao chachikhumicho. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Wina angathe kunena kuti Levi, amene amalandira chakhumi, anapereka chakhumicho kudzera mwa Abrahamu, Onani mutuwo |