Ahebri 7:24 - Buku Lopatulika24 koma Iye chifukwa kuti akhala Iye nthawi yosatha ali nao unsembe wosasinthika, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 koma Iye chifukwa kuti akhala Iye nthawi yosatha ali nao unsembe wosasinthika, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Koma Yesu ngwamuyaya, motero unsembe wake ngwosasinthika. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Koma Yesu popeza ndi wamuyaya, unsembe wake ndi wosatha. Onani mutuwo |