Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Ahebri 7:24 - Buku Lopatulika

24 koma Iye chifukwa kuti akhala Iye nthawi yosatha ali nao unsembe wosasinthika,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

24 koma Iye chifukwa kuti akhala Iye nthawi yosatha ali nao unsembe wosasinthika,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

24 Koma Yesu ngwamuyaya, motero unsembe wake ngwosasinthika.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

24 Koma Yesu popeza ndi wamuyaya, unsembe wake ndi wosatha.

Onani mutuwo Koperani




Ahebri 7:24
9 Mawu Ofanana  

Pamenepo khamulo linayankha Iye, Tidamva ife m'chilamulo kuti Khristu akhala kunthawi yonse; ndipo Inu munena bwanji, kuti Mwana wa Munthu ayenera kukwezedwa? Mwana wa Munthu amene ndani?


podziwa kuti Khristu anaukitsidwa kwa akufa, sadzafanso; imfa siichitanso ufumu pa Iye.


a iwo ali makolo, ndi kwa iwo anachokera Khristu, monga mwa thupi, ndiye Mulungu wa pamwamba pa zonse wolemekezeka kunthawi zonse. Amen.


Yesu Khristu ali yemweyo dzulo, ndi lero, ndi kunthawi zonse.


Pakuti chilamulo chimaika akulu a ansembe anthu, okhala nacho chifooko; koma mau a lumbirolo, amene anafika chitapita chilamulo, aika Mwana, woyesedwa wopanda chilema kunthawi zonse.


ndi Wamoyoyo; ndipo ndinali wakufa, ndipo taona, ndili wamoyo kufikira nthawi za nthawi, ndipo ndili nazo zofungulira za imfa ndi dziko la akufa.


Ndipo ndidzadziukitsira wansembe wokhulupirika, amene adzachita monga chimene chili mumtima mwanga ndi m'chifuniro changa; ndipo ndidzammangira nyumba yokhazikika, ndipo iyeyu adzayenda pamaso pa wodzozedwa wanga masiku onse.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa