Ahebri 7:23 - Buku Lopatulika23 Ndipo iwo ndiwo ambiri anakhala ansembe, popeza imfa idawaletsa asakhalebe; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Ndipo iwo ndiwo ambiri anakhala ansembe, popeza imfa idawaletsa asakhalebe; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Kusiyana kwina nkwakuti ansembe akale aja anali ambiri, chifukwa ankafa, sankatha kupitirira ndi udindo waowo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Tsono ansembe akale aja analipo ambiri, popeza imfa imawalepheretsa kupitiriza ntchitoyi. Onani mutuwo |