Ahebri 7:22 - Buku Lopatulika22 Momwemonso Yesu wakhala Nkhoswe ya pangano loposa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Momwemonso Yesu wakhala Nkhoswe ya pangano loposa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Kusiyana kokhudza lumbiroku kukutiwonetsa kuti Yesu ndi Nkhoswe yotsimikizira Chipangano choposa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Chifukwa cha lumbiroli, Yesu wakhala Nkhoswe ya Pangano lopambana. Onani mutuwo |