Ahebri 7:13 - Buku Lopatulika13 Pakuti Iye amene izi zineneka za Iye, akhala wa fuko lina, wa ili palibe munthu watumikira guwa la nsembe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Pakuti Iye amene izi zineneka za Iye, akhala wa fuko lina, wa ili palibe munthu watumikira guwa la nsembe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Ambuye athu, amene mauŵa akunena za Iwo, anali a fuko lina. Ndipo palibiretu wa fuko limeneli amene adatumikirapo ku guwa lansembe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Ambuye athu Yesu, amene mawuwa akunena za Iye, anali wa fuko lina, ndipo palibe aliyense wochokera fuko lakelo amene anatumikira pa guwa lansembe. Onani mutuwo |