Ahebri 6:16 - Buku Lopatulika16 Pakuti anthu amalumbira pa wamkulu; ndipo m'chitsutsano chao chilichonse lumbiro litsiriza kutsimikiza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Pakuti anthu amalumbira pa wamkulu; ndipo m'chitsutsano chao chilichonse lumbiro litsiriza kutsimikiza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Anthu amalumbira m'dzina la wina amene akuŵaposa, ndipo lumbiro lotere lotsimikizira mau, limathetsa kutsutsana konse pakati pao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Anthu amalumbira mʼdzina la wina amene akuwaposa, ndipo lumbiro lotere limatsimikizira zomwe zayankhulidwa ndi kuthetsa mikangano yonse. Onani mutuwo |