Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Ahebri 5:10 - Buku Lopatulika

10 wotchedwa ndi Mulungu mkulu wa ansembe monga mwa dongosolo la Melkizedeki.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 wotchedwa ndi Mulungu mkulu wa ansembe monga mwa dongosolo la Melkizedeki.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 ndipo Mulungu adamtchula mkulu wa ansembe onse, unsembe wake wonga uja wa Melkizedeki.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Ndipo Mulungu anamuyika kukhala Mkulu wa ansembe, monga mwa dongosolo la unsembe wa Melikizedeki.

Onani mutuwo Koperani




Ahebri 5:10
7 Mawu Ofanana  

Ndipo Melkizedeki mfumu ya ku Salemu, anatuluka nao mkate ndi vinyo: iye ndiye wansembe wa Mulungu Wamkulukulu.


Yehova walumbira, ndipo sadzasintha, Inu ndinu wansembe kosatha monga mwa chilongosoko cha Melkizedeki.


Potero kudamuyenera kufanizidwa ndi abale m'zonse, kuti akadzakhala mkulu wa ansembe wachifundo ndi wokhulupirika m'zinthu za kwa Mulungu, kuti apereke dipo la zoipa za anthu.


Potero, abale oyera mtima, olandirana nao maitanidwe akumwamba, lingirirani za Mtumwi ndi Mkulu wa ansembe wa chivomerezo chathu, Yesu;


Za iye tili nao mau ambiri kuwanena, ndi otivuta powatanthauzira, popeza mwagontha m'makutu.


m'mene Yesu mtsogoleri analowamo chifukwa cha ife, atakhala mkulu wa ansembe nthawi yosatha monga mwa dongosolo la Melkizedeki.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa