Ahebri 5:10 - Buku Lopatulika10 wotchedwa ndi Mulungu mkulu wa ansembe monga mwa dongosolo la Melkizedeki. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 wotchedwa ndi Mulungu mkulu wa ansembe monga mwa dongosolo la Melkizedeki. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 ndipo Mulungu adamtchula mkulu wa ansembe onse, unsembe wake wonga uja wa Melkizedeki. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Ndipo Mulungu anamuyika kukhala Mkulu wa ansembe, monga mwa dongosolo la unsembe wa Melikizedeki. Onani mutuwo |