Ahebri 2:18 - Buku Lopatulika18 Pakuti popeza adamva zowawa, poyesedwa yekha, akhoza kuthandiza iwo amene ayesedwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Pakuti popeza adamva zowawa, poyesedwa yekha, akhoza kuthandiza iwo amene ayesedwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Tsono popeza kuti iye yemwe adazunzikapo ndi kuyesedwapo, ndiye kuti angathe kuŵathandiza anthu amene amayesedwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Popeza Iye mwini anamva zowawa pamene anayesedwa, Iyeyo angathe kuthandiza amene akuyesedwanso. Onani mutuwo |