Ahebri 2:13 - Buku Lopatulika13 Ndiponso, Ndidzamtama Iye. Ndiponso, Taonani, Ine ndi ana amene Mulungu anandipatsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndiponso, Ndidzamtama Iye. Ndiponso, Taonani, Ine ndi ana amene Mulungu anandipatsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Amanenanso kuti, “Ndidzakhulupirira Mulungu.” Penanso amanena kuti, “Ine ndili pano, pamodzi ndi ana amene Mulungu adandipatsa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Ndiponso, “Ine ndidzakhulupirira Iyeyo.” Ndiponso Iye akuti, “Ine ndili pano pamodzi ndi ana amene Mulungu wandipatsa.” Onani mutuwo |