Ahebri 2:12 - Buku Lopatulika12 Ndi kuti, Ndidzalalikira dzina lanu kwa abale anga, pakati pa Mpingo ndidzakuimbirani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndi kuti, Ndidzalalikira dzina lanu kwa abale anga, pakati pa Mpingo ndidzakuimbirani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 ponena mau akuti, “Ndidzasimbira abale anga za dzina lanu. Ndidzakutamandani pa msonkhano wa anthu anu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Iye akuti, “Ine ndidzawuza abale anga za dzina lanu. Ndidzakuyimbirani nyimbo zamatamando pamaso pa mpingo.” Onani mutuwo |