Ahebri 12:13 - Buku Lopatulika13 ndipo lambulani miseu yolunjika yoyendamo mapazi anu, kuti chotsimphinacho chisapatulidwe m'njira, koma chichiritsidwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 ndipo lambulani miseu yolunjika yoyendamo mapazi anu, kuti chotsimphinacho chisapatulidwe m'njira, koma chichiritsidwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Muziyenda m'njira zoongoka, kuti miyendo yopunduka isagweduke, koma ichiritsidwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Muziyenda mʼnjira zowongoka, kuti iwo amene akukutsatirani ngakhale ndi olumala ndi ofowoka asapunthwe ndi kugwa koma adzilimbikitsidwa. Onani mutuwo |