Ahebri 11:14 - Buku Lopatulika14 Pakuti iwo akunena zotere aonetserapo kuti alikufuna dziko likhale lao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Pakuti iwo akunena zotere aonetserapo kuti alikufuna dziko likhale lao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Paja anthu olankhula motere, amaonekeratu kuti akufunafuna malo ao enieni okhazikikamo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Anthu amene amanena zinthu zotere amaonekeratu kuti akufuna dziko lawo lenileni. Onani mutuwo |