Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Ahebri 11:14 - Buku Lopatulika

14 Pakuti iwo akunena zotere aonetserapo kuti alikufuna dziko likhale lao.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 Pakuti iwo akunena zotere aonetserapo kuti alikufuna dziko likhale lao.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

14 Paja anthu olankhula motere, amaonekeratu kuti akufunafuna malo ao enieni okhazikikamo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 Anthu amene amanena zinthu zotere amaonekeratu kuti akufuna dziko lawo lenileni.

Onani mutuwo Koperani




Ahebri 11:14
9 Mawu Ofanana  

Ndipo anaona mwana, ndi Mose anamutcha dzina lake Geresomo; pakuti anati, Ndakhala mlendo m'dziko la eni.


popeza sitipenyerera zinthu zooneka, koma zinthu zosaoneka; pakuti zinthu zooneka zili za nthawi, koma zinthu zosaoneka zili zosatha.


Koma ndipanidwa nazo ziwirizi, pokhala nacho cholakalaka cha kuchoka kukhala ndi Khristu, ndiko kwabwino koposaposatu;


Iwo onse adamwalira m'chikhulupiriro, osalandira malonjezano, komatu adawaona ndi kuwalankhula kutali, navomereza kuti ali alendo ndi ogonera padziko.


Ndipotu akadakumbukira lijalo adatulukamo akadaona njira yakubwerera nayo.


Koma tsopano akhumba lina loposa, ndilo la mu Mwamba; mwa ichi Mulungu sachita manyazi nao poitanidwa Mulungu wao; pakuti adawakonzera mzinda.


Pakuti pano tilibe mzinda wokhalitsa, komatu tifunafuna ulinkudzawo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa