Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Ahebri 11:15 - Buku Lopatulika

15 Ndipotu akadakumbukira lijalo adatulukamo akadaona njira yakubwerera nayo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Ndipotu akadakumbukira lijalo adatulukamo akadaona njira yakubwera nayo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Akadakhala kuti ankaganizirako za kudziko kumene adaachokera, bwenzi atapeza danga lakuti abwerere kwakaleko.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Akanakhala kuti akuganizira za dziko limene analisiya akanapeza mpata obwerera kwawo.

Onani mutuwo Koperani




Ahebri 11:15
7 Mawu Ofanana  

Ndipo Tera anatenga Abramu mwana wake wamwamuna, ndi Loti mwana wa Harani, mwana wake wamwamuna, ndi Sarai mpongozi wake, mkazi wa mwana wake Abramu; ndipo anatuluka pamodzi nao ku Uri wa kwa Akaldeya kuti amuke ku dziko la Kanani, ndipo anafika ku Harani, nakhala kumeneko.


Ndipo munali njala m'dzikomo, ndipo anatsikira Abramu ku Ejipito kukakhala kumeneko, chifukwa kuti njala inali yaikulu m'dziko m'menemo.


Koma udzanke ku dziko langa, kwa abale anga, ndi kumtengera mwana wanga Isaki mkazi.


ndipo ananka nazo zoweta zake zonse, ndi chuma chake chonse anachisonkhanitsa, zoweta zake anaziona mu Padanaramu, kuti anke kwa Isaki atate wake ku dziko la Kanani.


Pakuti iwo akunena zotere aonetserapo kuti alikufuna dziko likhale lao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa