Ahebri 10:32 - Buku Lopatulika32 Koma tadzikumbutsani masiku akale, m'menemo mutaunikidwa mudapirira chitsutsano chachikulu cha zowawa; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 Koma tadzikumbutsani masiku akale, m'menemo mutaunikidwa mudapirira chitsutsano chachikulu cha zowawa; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 Kumbukirani masiku akale aja mutangolandira kuŵala chatsopano. Pa nthaŵi imene ija mudaalimbana ndi mazunzo ambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 Kumbukirani masiku akale aja mutangowunikiridwa chatsopano, pa nthawi imeneyi munapirira zowawa zambiri. Onani mutuwo |