Ahebri 10:33 - Buku Lopatulika33 pena pochitidwa chinthu chooneredwa mwa matonzo ndi zisautso; penanso polawana nao iwo ochitidwa zotere. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201433 pena pochitidwa chinthu chooneredwa mwa matonzo ndi zisautso; penanso polawana nao iwo ochitidwa zotere. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa33 Mwina ankakunyozani ndi kukuchitani chipongwe, anthu akuwonerera. Mwinanso munkamva nawo zoŵaŵa amene ankasautsidwa motero. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero33 Nthawi zina ankakunyozani pagulu ndi kukuzunzani. Nthawi zina munkamva zowawa pamodzi ndi amene ankasautsidwa chotere. Onani mutuwo |