Ahebri 10:21 - Buku Lopatulika21 ndipo popeza tili naye wansembe wamkulu wosunga nyumba ya Mulungu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 ndipo popeza tili naye wansembe wamkulu wosunga nyumba ya Mulungu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Ndiponso tili ndi Wansembe wamkulu woyang'anira nyumba ya Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Ndiponso tili ndi wansembe wamkulu woyangʼanira nyumba ya Mulungu. Onani mutuwo |