Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Ahebri 10:21 - Buku Lopatulika

21 ndipo popeza tili naye wansembe wamkulu wosunga nyumba ya Mulungu;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

21 ndipo popeza tili naye wansembe wamkulu wosunga nyumba ya Mulungu;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

21 Ndiponso tili ndi Wansembe wamkulu woyang'anira nyumba ya Mulungu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

21 Ndiponso tili ndi wansembe wamkulu woyangʼanira nyumba ya Mulungu.

Onani mutuwo Koperani




Ahebri 10:21
12 Mawu Ofanana  

Ndiponso Ine ndinena kwa iwe, kuti iwe ndiwe Petro, ndipo pa thanthwe ili ndidzakhazika Mpingo wanga; ndipo makomo a dziko la akufa sadzagonjetsa uwo.


kuti udziwe kuyenedwa kwake pokhala m'nyumba ya Mulungu, ndiye Mpingo wa Mulungu wamoyo, mzati ndi mchirikizo wa choonadi.


Potero kudamuyenera kufanizidwa ndi abale m'zonse, kuti akadzakhala mkulu wa ansembe wachifundo ndi wokhulupirika m'zinthu za kwa Mulungu, kuti apereke dipo la zoipa za anthu.


Potero, abale oyera mtima, olandirana nao maitanidwe akumwamba, lingirirani za Mtumwi ndi Mkulu wa ansembe wa chivomerezo chathu, Yesu;


m'mene Yesu mtsogoleri analowamo chifukwa cha ife, atakhala mkulu wa ansembe nthawi yosatha monga mwa dongosolo la Melkizedeki.


Pakuti mkulu wa ansembe wotere anatiyenera ife, woyera mtima, wopanda choipa, wosadetsedwa, wosiyana ndi ochimwa, wakukhala wopitirira miyamba;


Koma mutu wa izi tanenazi ndi uwu: Tili naye Mkulu wa ansembe wotere, amene anakhala padzanja lamanja la mpando wachifumu wa Ukulu mu Kumwamba,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa